“Nkhani yeniyeni apa ndi ufulu
wokhala mayi
.

Amayi masiku ano awirikiza pankhani ya yopitsa
mtsogolo ufulu wokhala mayi pakati pa magulu omwe apanga tsankho ndi anthu a
akazi! Izi nzofunika makaka ku ntchito, koma osati ku
tchalitchi!”

“Pepani, anzanga!

Nkhani ya ufulu ya amayi ndi
yofunuika kwambiri mu mpingo
. Kuti mpingo uyende bwino ndi kutukuka
nkhaniyi tiyiganizire mozama ndi mwachilungamo!

Mzoonani kuti nkhondo ya
amayi pomenyera ufulu wawo ya tithandiza amayi kundikira kuti amainso ali ndi
gawo lofunika mu ntchito za mpingo. Nkhondoyi si yachilendo popoza maziko ake
ali mu mbiri ya mpingo.”

Nzachisoni kuti Tchalitchi chinatengera
chikhalidwe cha mitundu yambiri yomwe imatenga amayi ngati anthu operewedwa mu
umunthu wawo!

“INU AMAYI mufuna kusintha
chiphunzitso cha mpinzo ncholinga choti zinthu zizikukomera mbali yanu
.

Koma ife tisankha kutsatiza chimphunzitso choyera cha mpingo chomwe
sichisintha.

Thalitchi silingasinthe malumulo ake kuti liwoneke lotukuka
kapena kukondweretsa amayi omwe afuna kufanana ndi anthu
amuna!”

“Kulakwa!

Ayi, sitisowa kusintha malamulo a mpingo.

Chomwe chisowa kusintha ndi maphunziro ena a mpingo amene amakuza
chizolowezi cha tsankho lopondereza amayi.

Tiyenera kuchotsa mfundo
zonse zimene zimaika khungu m’maso mwa atsogoleri a mpingo amene amatanthauzira
chiphunzitso cha mpingo mokondera popondereza amayi. Izi zimabweretsa khungu
lomwe likutilepheretsa kumvetsa tanthauzo lenileni la Malembo Woyera.

Mchifukwa chiyani tikutsutsana ndi uphunzitsi wa mpingo wa
mtsankho
Mafunso
apafupipafupi
Zina?
kusintha kwa
chikalidwe
mfundombirikumvera
kwenikweni
nthumanzi ya
chikhulupiriro
ufulu wokhala
mayi?
uphunzitsi
wosatsutsika?
kudalilika?kumvera?kederera?
Kodi ‘maufulu’ a aKatolika
mtchalitchi ndi ati?
Muli ndi mafunso? __Maganizo ena?
__Ndemanga?