Tamasuludwa ku Tsankho

Zoonadi, kalelo Mpingo unkakana kudzodza amayi kuti akhale ansembe.
Koma chifukwa?
Polingalira machitidwe a mpingo kalelo, tiyeneranso kufufuza zifukwa zoyenra zomwe anthu ankaganira kuti amayi asakhale ansembe. Chifukwa chiyani amai samadzodzedwa unsembe
Koma kwa amayi, akafufuza amaona kuti zifukwazi nzokhumudwitsa.
Amayi ankakanizidwa kulowa unsembe pazifukwa zopanda pake.



The evil of prejudice

Mfundo zitatu zopondereza zimalepheretsa amayi kutumikira muunsembe.

1. 1. Amayi ankaonebwa ngati otsalira mu zonse: mphamvu za thupi, mu mzeru ndi mu kulimba mtima.
Amkatero popeza ankakhulupira kuti ku mbewu yomwe imabweretsa mwa wa mamuna ‘mwakhazikitsidwa’ chimanga mtundu, choncho amayi ankaonedwa ngati anthu operewedwa.
Machdule, Amayi ankatengedwa ngat anthu operewedwa.

2. Popeza Eva adagwetsa mtundu wa anthu, mkazi aliyense ankaganiziridwa kuti ali ndi themebrero la Eva.
Women were marked as sinful creatures.

3. Anthu amaganiza kuti mayi akakhala akasamba ndiye kuti ndiwodetsedwa.
Poonedwa ngati anthu odetsedwa amayi samaloredwa kutenga mbali pa mwambo wothira msembe










 

Nthawi zonse Mpingo usowa kudzimasula mu mtcichidwe wa tsankho womwe umaonengwa ziphunzitso ndi zizolewezi zabwino mu mpingo.




Kufikira m’chaka cha 1854 a Papa amkaphunzitsa kuti ukapolo ngovomerezeka kwa Mulungu, koma tsopano Mpingo umaletsa ukapolo.



The Church has made many similar mistakes throughout its history.

Amayi a lero ayenera kumasulidwa mu la chimpunzitso cha tsankho mu mpingo chomwe chimaletsa amayi kutenga mbali mu utumiki wa unsembe umene Mulungu adawaitainira.


 
  
Zina

1

2

3

4

5

6

7

obatizidwa

olimbikitsidwa

omasulidwa

odzodzedwa

ovomerezedwa

othandizidwa

oitanidwa