Unsembe umodzi mwa Khristu


Zzikukwa zisanu m’mziwiri zoyambirira zoti amayi ngoyera kudzodzedwa Unsembe

Nchipangano Chakale anthu wakazi samawerengerenga ngati anthu monga anthu wamuna. Popeza amayi samkaumbala samawerengedwa ngati anthu osankhidwa ndi Mulungu. Choncho amayi analibe ufulu wopereka msembe zao paokha. Thawi zonse ntchito zao pa zachipembedzo zimakhala zongothandiza amuna omwe ankawapondereza.
The mystery of baptism

Ambuye Yesu anasudzula nchitidwe wopondreza amayi
Mzimayi aliyense wobatizidwa amasanduka chifanizo cha Ambuye Yesu, chimodzimodzi mu ubatizo wa amuna. ““Onse amene abatizidwa mwa Khristu, atengere chifanizo cha Khristu. Palibenso tsankho pakati pa Ayuda ndi anthu ena onse, kapolo ndi mfulu, mamuna ndi mkazi .” Galatians 3,28
Choncho mkazi aliyense wobatizidwa amatenga mbali mopanda kutsaliza mu unsembe wa Khristu, mu utumiki wake mu ufumu ndi ulaliki.


Ubatizo ndi mphatso yomwe yimatiyeneretsa kulandira masakramenti onse, ndi unsembe omwe.


Zina?

1

2

3

4

5

6

7

obatizidwa

olimbikitsidwa

omasulidwa

odzodzedwa

ovomerezedwa

othandizika

oitanidwa