Pali pafufupi mfundo zizanu ndi ziwiri yeneretsa amayi kudzodzedwa Unsembe

1. Unsembe umodzi mwa Yesu

Paubatizo wawo akazi ndio amuna amasanduaka atumuki ofanana mu unsembe wa Khristu. Kufananaku kuli chimodzimozdi pa kudzodzedwa unsembe. click!

2. Apatsidwa mphamvu ya kutsogelera

Pa khomaliro otsiliza Khrist anapreka mphamvu mofanana kwa amai ndi abambo. Choncho onsewa atha kulandira mphmvu zosandulitsa ukalistia. click!

3. Chikkalidwe cha mafuko cha tsamkho

Chizolowezi choletsa amai kudzodzedwa unsembe chidambika ndi tsakho lomwe linali ndi mbali zitatu. Tankholi lidapotoza kuganiza kwa a tsogoleri a mp[ingo pa nkhaniyi. click!

4. Amayi akhala ma dikoni

Pachiyambi mpaka chaka cha 900 Mpingo umapereka undindo wosapereweza kwa amayi osanduliza ukalistia podzodza amayi u dikoni. Iziti zikusonyeza kuti mayi athanso kudzodzedwa unsembe. click!

5. Zoyenertsa mai kudzodwa unsembe zakhala zilipo nthawi yomwe mpingo udali nchizolowezi cha chete.

Mwachitsanzo chizolewesi cholemeza amayi Maria ngati wansembe. Izitu zikutanthuza kuti, naga ‘mkulingalira kwa akhristu’, It shows that, according to the ‘sense of the faithful’, kudzera mchitsanzo cha amayi Maria mtsakho lotchingiriza amayi ku unsembe ndi longonjetsedwa kale.click!

6. A Khristu amabiri mziko lapansi amavomereza unsembe wa amayi.

Pambuyo pa kusinkhasinkha ndi ma mapepmhero a Kristu a mpipingo ina amadzodza mai oyenerera unsembe. Ngakhale kuti si zonse zomwe mipingo ina imachita nzovomerezeka kwa akatolika, zimvano cha a khristu a mpipingo ya mbiri pa unsembe wa amayi sikutsindika mfundo unsembe wa amai ngolingana ndi chifuniro cha Khristu. click!

7. Amayinso, ponena mwa tchutchutchu, ngoitanidwa ku unsembe.

Popeza kuti amayi ambiri wodzilemekeza amamva mu mtima mwawo kuitanidwa ku unsembe izi nzisoneza za chifunuiro cha Mzimu Woyera chomwe ife sitiyenera kuchikana. click!


Po tsiliza: palibe zenizeni mwa mfundo zomwe zimaperekedwa pa tsankho lomwe limarepheretsa ami kulowa unsembe, ndiponso mfumdo zambirizogwirizana chikhululupiriro cha chikatolika zikukomera maganizo a unsembe wa amayi!


Nanganso bwanji uphunzi wa a Papa ukutchingiriza unsembe wa a mayi?


Werengani mafunso amene amabwera pafupipafupi!



Zina