Zokhumudwitsa mzakuti mkoletsedwa kukambirananso mfundo zomwe zimabweretsa tsankho lotchingiriza Amayi ku unsembe. Akulu akulu woyang’ira maphunzitso a Mpingo a akupondereza ufulu wa Amayi..
Mukafuna kuziwa zambiri za zomwe tikutsutsa mpingo pa nkhaniyi, werengani zomwe tatonkha pa za maganizo a anthu osiyanasiyana.
Pano tikamba Mfundo zina mosabisa.
1. Ambuye Yesu anapereka kwa Amai gawo la utumki chimodzimodi ndi abambo ndinso anawalimbiotsa powapatsa Amayi, monga bambo, mphamvu zosandulitsa Ukalistia,. | ![]() |
![]() | 2. Until at Kwa zaka 900 . |
“Komadi ku Roma analamula kuti nkhaniyi nchimphunzitso chomwe a Khritsu alibe mphamvu zotsutsa?!”




